Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa Thru the Bible Chichewa
-
- Religion & Spirituality
Pologalamu ya Tisanthule Baibulo ndi gawo limodzi lautumiki, ophunzitsa Baibulo, otchedwa ulendo m??baibulo (Thru the Bible). Mndandanda wamapogalamuwu unakonzedwa ndi Dr. J. Vernon McGee ndipo unatanthauzidwa mu zilankhulo zoposa zana zimodzi (100). Zinakonzedwa kuti pologalamu imodzi idzikhala ya mphindi makumi atatu (30) ndipo kuti pomaliza zidzathe kuthandiza omvera kumvetsetsa Baibulo lonse. Ndipo pakali pano mapologalamu onsewa tawaika pamakina a Intaneti. Ndife oyamika kuti mwasankha kuphunzira zambiri zokhudza mau a Mulungu kudzera mmapologalamuwa. Tikukulimbikitsani kuti mudzimvera pologalamu imodzi patsiku kuyambira lolemba mpaka lachisanu. Ngati mungakwanitse kutsatira ndondomekoyi, pakutha kwa zaka zisanu mudzakhala kuti mwawerenga Baibulo lonse.
-
Chiyambi Cha Bukhu La Yoswa, Yoswa Atenga Udindo Ndi
-
Nyimbo Ya Mose, Mdalitso Ndi Imfa Yake Ulamuliro Wake
-
Moyo Ndi Zabwino Kulinganiza Ndi Imfa Ndi Zoyipa; Kusintha Kwa Utsogoleri
-
-
Malonjezo A Mulungu; Madalitso Pakumvera Ndi Tsoka Pa kusamvera
-
Kukwapula Wolakwa, Kuteteza Mkazi Wamasiye, Chilango Cha Amaleke, Ndi Chopereka Cha Zipatso Zoyamba